Isaiah 14:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta Wamphamvuzonse ndiye watsimikiza kuti zimenezi zichitike, nanga ndaninso angathe kumletsa? Dzanja lake nlotambalitsa, nanga ndaninso angalibweze?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yehova wa makamu wapanga uphungu, ndani adzauleketsa? Ndi dzanja lake latambasulidwa, ndani adzalibweza?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza, ndipo ndani angamuletse? Dzanja lake latambasulidwa ndipo ndani angalibweze?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yehova wa makamu wapanga uphungu, ndani adzauleketsa? ndi dzanja lace latambasulidwa, ndani adzalibweza?