Isaiah 14:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi tidzaŵayankhanji amithenga a ku Filistiyawo? Tidzati, “Chauta adakhazikitsa kale Ziyoni, ndipo mu mzinda umenewu anthu ake ozunzika amapeza populumukira.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo adzayankhanji amithenga a amitundu? Kuti Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo m'menemo anthu ake ovutidwa adzaona pobisalira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi tidzawayankha chiyani amithenga a ku Filisitiya? “Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo mu mzinda wakewu, anthu ozunzika apeza populumukira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo adzayankhanji amithenga a amitundu? Kuti Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo m'menemo anthu ace obvutidwa adzaona pobisalira.