Isaiah 14:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero mudzanyodola mfumu ya ku Babiloni, mudzati, “Watha bwanji wopsinja uja? Kwatha bwanji kudzikuza kwake kuja?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamenepo udzaimbira mfumu ya ku Babiloni nyimbo iyi yanchinchi, ndi kuti, Wovuta wathadi? Mudzi wagolide wathadi!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mudzayankhula monyogodola mfumu ya Babuloni kuti, Wopsinja uja watha! Ukali wake uja watha!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pamenepo udzayimbira mfumu ya ku Babulo nyimbo iyi yancinci, ndi kuti, Wobvuta wathadi! mudzi wagolidi wathadi!