Isaiah 14:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwowo ankakantha mitundu ya anthu mokwiya pomaŵamenya kosalekeza. Ankalamulira mitundu ya anthu mwaukali ndi kumaŵazunza kosalekeza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wokantha anthu mwaukali kuwakantha chikanthire, wolamulira amitundu mokwiya, angosautsidwa wopanda womlanditsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mfumu ya ku Babuloni inkakantha mitundu ya anthu mwaukali powamenya kosalekeza, Iyo inkagonjetsa anthu a mitundu ina mwaukali ndikuwazunza kosalekeza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wokantha anthu mwaukali kuwakantha cikanthire, wolamulira amitundu mokwiya, angosautsidwa wopanda womlanditsa.