Isaiah 14:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Dziko lonse lapansi lapumula, tsopano lakhala bata, ndipo anthu akuimba mokondwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Dziko lonse lapuma, lili duu; iwo ayamba kuimba nyimbo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma tsopano mayiko onse ali pa mpumulo ndi pa mtendere; ndipo akuyimba mokondwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Dziko lonse lapuma, liri du; iwo ayamba kuyimba nyimbo,