Isaiah 14:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mitengo ya paini ikukondwerera kugwa kwa Babiloni. Mikungudza ya ku Lebanoni ikuti, ‘Chigwetsedwere chako pansi, mfumu iwe, palibe wina amene adabwera kudzatigwetsa.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inde, milombwa ikondwera ndi iwe, ndi mikungudza ya Lebanoni, ndi kunena, Chigwetsere iwe pansi, palibe wokwera kudzatidula ife.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale mitengo ya payini ndi mikungudza ya ku Lebanoni ikuyimba za iwe mokondwa ndipo ikuti, “Chigwetsedwere chako pansi, palibe wina anabwera kudzatigwetsa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inde, milombwa ikondwera ndi iwe, ndi mikungudza ya Lebano, ndi kunena, Cigwetsere iwe pansi, palibe wokwera kudzatidula ife.