Isaiah 2:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nazi zinthu zokhudza Yuda ndi Yerusalemu, zimene Yesaya, mwana wa Amozi, adaziwona m'masomphenya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau amene Yesaya mwana wa Amozi anaona, onena za Yuda ndi Yerusalemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nazi zinthu zokhudza Yuda ndi Yerusalemu, zimene Yesaya mwana wa Amozi anaziona mʼmasomphenya:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau amene Yesaya mwana wa Amozi anaona, onena za Yuda ndi Yerusalemu.