Isaiah 2:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu zidzukulu za Yakobe, tiyeni tiyende m'kuŵala kwa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inu a nyumba ya Yakobo, tiyeni, tiyende m'kuwala kwa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu nyumba ya Yakobo, bwerani, tiyeni tiyende mʼkuwala kwa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inu a nyumba ya Yakobo, tiyeni, tiyende m'kuwala kwa Yehova.