Isaiah 23:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo adati, “Simudzakondwanso, inu anthu a mu mzinda wa Sidoni, mudzapanikizidwa, ndipo ngakhale muthaŵire ku Kitimu, nkumeneko komwe simukapeza mpumulo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Iye anati, Iwe sudzakondwanso konse, iwe namwali wovutidwa, mwanawamkazi wa Sidoni; uka, oloka kunka ku Kitimu; ngakhale kumeneko iwe sudzapumai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anati, “Simudzakondwanso konse, inu anthu opanikizidwa a ku Sidoni, tsopano wamphwanyidwa! “Ngakhale muwolokere ku Kitimu, kumeneko simukapezako mpumulo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Iye anati, Iwe sudzakondwanso konse, iwe namwali wobvutidwa, mwanawamkazi wa Zidoni; uka, oloka kunka ku Kitimu; ngakhale kumeneko iwe sudzapumai.