Isaiah 23:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma phindu lake ndi malipiro ake adzazipereka kwa Chauta. Sadzachita nazo kaligwiritsa kapena kuzikundika, koma adzazipereka kwa otumikira Chauta, kuti agule zakudya zambiri ndi zovala zokongola.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Malonda ake ndi mphotho yake zidzakhala zopatulikira Yehova; sizidzasungidwa kapena kuikidwa; chifukwa malonda ake adzakhala kwa iwo, amene akhala pamaso pa Yehova, kuti adye mokwana, navale chaulemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma phindu lake ndi malipiro ake adzazipereka kwa Yehova; sadzazikundika kapena kuzisunga. Phindu lake lidzapita kwa mtumiki wa Yehova kuti agule zakudya zambiri ndi zovala zokongola.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Malonda ace ndi mphotho yace zidzakhala zopatulikira Yehova; sizidzasungidwa kapena kuikidwa; cifukwa malonda ace adzakhala kwa iwo, amene akhala pamaso pa Yehova, kuti adye mokwana, nabvale caulemu.