Isaiah 26:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Chauta ndinu Wolungama, mumasalaza njira ya munthu womvera inu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Njira ya wolungama ili njira yoongoka; Inu amene muli woongoka, mukonza njira ya wolungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Njira ya munthu wolungama ndi yosalaza, Inu Wolungamayo, mumasalaza njira ya wolungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Njira ya wolungama iri njira yoongoka; Inu amene muli woongoka, mukonza njira ya wolungama.