Isaiah 28:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adaakuuzani kuti, “Malo opumulira ndi ano, otopa apumule, malo ousira ndi ano,” koma inu simudamvere.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amene ananena nao, Uku ndi kupuma, mupumitsa wolema, ndi apa ndi potsitsimutsa, koma iwo anakana kumva.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
anakuwuzani kuti, “Malo opumulira ndi ano, otopa apumule, malo owusira ndi ano.” Koma inu simunamvere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
amene ananena nao, Uku ndi kupuma, mupumitsa wolema, ndi apa ndi potsitsimutsa, koma iwo anakana kumva.