Isaiah 28:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Oweruza adzaŵapatsa mtima wachilungamo. Adzaŵalimbitsa mtima onse amene amalimbana ndi adani pa zipata za mzinda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo adzakhala mzimu wa chiweruziro kwa oweruza milandu, ndi mphamvu kwa iwo amene abweza nkhondo pachipata.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye adzapereka mtima wachilungamo kwa oweruza, adzakhala chilimbikitso kwa amene amabweza adani pa zipata za mzinda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo adzakhala mzimu wa ciweruziro kwa oweruza mirandu, ndi mphamvu kwa iwo amene abweza nkhondo pacipata.