Isaiah 3:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsopano Chauta afuna kuyambapo mlandu, wakonzeka kale kuweruza anthu ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova aimirira kuti atsutsane, naimiriranso kuti aweruze mitundu ya anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova wakhala pamalo pake mʼbwalo la milandu; wakonzeka kuti aweruze anthu ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova aimirira kuti atsutsane, naimiriranso kuti aweruze mitundu ya anthu.