Isaiah 3:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwe Yerusalemu, anthu ako aamuna adzaphedwa ndi lupanga, ndipo anthu ako amphamvu adzafera ku nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amuna ako adzagwa ndi lupanga, ndi wamphamvu wako m'nkhondo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwe Yerusalemu anthu ako aamuna adzaphedwa ndi lupanga, asilikali ako adzafera ku nkhondo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amuna ako adzagwa ndi lupanga, ndi wamphamvu wako m'nkhondo.