Isaiah 30:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene Mulungu adzakhala akuŵalanga adani aja, anthu ake adzakhala akuvina ndi ting'oma ndi azeze. Mulungu mwini adzamenyana ndi Aasiriya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo nthawi zonse Yehova adzawakantha ndi ndodo yosankhikayo, padzamveka mangaka ndi zeze; ndi m'nkhondo zothunyanathunyana, Iye adzamenyana nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova akamadzalanga adani ake ndi ndodo, anthu ake adzakhala akuvina nyimbo zoyimbira matambolini ndi azeze, Yehova ndiye ati adzamenyane ndi Asiriyawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo nthawi zonse Yehova adze vakantha ndi ndodo yosankhikayo, padzamveka mangaka ndi zeze; ndi m'nkhondo zothunyana-thunyana, Iye adzamenyana nao.