Isaiah 30:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale kuti nduna zake zafika kale ku Zowani, ndipo akazembe ake afika kale ku Hanesi,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti akalonga ake ali pa Zowani, ndi mithenga yake yafika ku Hanesi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale kuti nduna zawo zili ku Zowani, ndipo akazembe awo afika kale ku Hanesi,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti akalonga ace ali pa Zaani, ndi mithenga yace yafika ku Hanesi.