Isaiah 32:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma munthu wa mtima wabwino amalingalira zabwino, ndipo amalimbikira kuchita zabwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mfulu aganizira zaufulu, nakhazikika m'zaufulu zomwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma munthu wolemekezeka amalingaliranso kuchita zinthu zabwino, Iye amakhazikika pa zinthu zabwinozo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mfulu aganizira zaufulu, nakhazikika m'zaufulu zomwe.