Isaiah 33:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu mumaganiza zachabechabe, ndipo zonse zimene mumachita nzopandapake. Zotuluka m'kamwa mwanu zili ngati moto umene udzakuwonongani inu nomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inu mudzatenga pakati ndi mungu, mudzabala ziputu; mpweya wanu ndi moto umene udzakumalizani inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zolingalira zanu nʼzachabechabe ngati udzu wamanyowa. Mpweya wamoto udzakupserezani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inu mudzatenga pakati ndi mungu, mudzabala ziputu; mpweya wanu ndi moto umene udzakumarizani inu.