Isaiah 33:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a mitundu ina adzakhala ngati miyala yotenthedwa popanga njereza, adzakhala ngati minga yodula, yotenthedwa pamoto.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mitundu ya anthu idzanga potentha miyala yanjeresa; monga minga yodulidwa, nitenthedwa ndi moto.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a mitundu ina adzatenthedwa ngati miyala ya njereza; ndi ngati minga yodulidwa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mitundu ya anthu idzanga potentha miyala yanjeresa; monga minga yodulidwa, nitenthedwa ndi moto.