Isaiah 33:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Inu amene muli kutali, imvani zimene ndachita. Inu amene muli pafupi, dziŵani mphamvu zanga.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Imvani inu amene muli kutali, chimene ndachita ndi inu; amene muli pafupi, vomerezani mphamvu zanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu amene muli kutali, imvani zimene ndachita; inu amene muli pafupi, dziwani mphamvu zanga
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Imvani inu amene muli kutari, cimene ndacita ndi inuamene muli pafupi, bvomerezani mphamvu zanga,