Isaiah 33:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi imeneyo mudzayang'ana mfumu yooneka mokongola, ndipo mudzaona dziko labwino lotambasukira kutali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maso ako adzaona mfumu m'kukongola kwake; iwo adzaona dziko lakutali.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi imeneyo maso a ana adzaona mfumu ya maonekedwe wokongola ndi kuona dziko lotambasukira kutali.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maso ako adzaona mfumu m'kukongola kwace; iwo adzaona dziko lakutari.