Isaiah 33:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mumtima mwanu muzidzalingalira zimene zinkakuwopsani kale. Muzidzati, “Ali kuti wokhometsa msonkho uja?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wako udzaganizira zoopsa; mlembi ali kuti? Ali kuti iye amene anayesa msonkho? Ali kuti iye amene anawerenga nsanja?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mu mtima mwanu muzidzalingalira zoopsa zinachitika kale zija: “Ali kuti mkulu wa Asilikali uja? Ali kuti wokhometsa misonkho uja? Ali kuti mkulu woyangʼanira nsanja?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wako udzaganizira zoopsya; mlembi ali kuti? ali kuti iye amene anayesa msonkho? ali kuti iye amene anawerenga nsanja?