Isaiah 33:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mukatulutsa liwu lanu longa bingu, mitundu ya anthu imathaŵa. Inu mukadzambatuka, mitundu ya anthu imabalalika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pa mau a phokoso mitundu ya anthu yathawa; ponyamuka iwe amitundu abalalika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mukatulutsa liwu lanu longa bingu mitundu ya anthu imathawa; pamene Inu mwadzambatuka mitundu ya anthu imabalalika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pa mau a phokoso mitundu ya anthu yathawa; ponyamuka iwe amitundu abalalika,