Isaiah 33:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amakundika zokunkha monga m'mene zimachitira ziwala. Anthu amalumphira zofunkhazo monga m'mene limachitira dzombe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo zofunkha zanu zidzasonkhanitsidwa, monga ziwala zisonkhana; monga dzombe atumpha, iwo adzatumpha pa izo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zofunkha za ku nkhondo za mitundu ina Aisraeli adzazisonkhanitsa ngati mmene limachitira dzombe. Iwo adzalumphira zofunkhazo monga mmene limachitira dzombe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo zofunkha zanu zidzasonkhanitsidwa, monga ziwala zisonkhana; monga madzombe atumpha, iwo adzatumpha pa izo.