Isaiah 33:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta ndi wolemekezeka kwambiri, pakuti akukhala pamwamba pa zonse. Adzadzaza mzinda wa Ziyoni ndi chilungamo ndi ungwiro.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova wakwezedwa; pakuti akhala kumwamba; Iye wadzaza Ziyoni ndi chiweruzo ndi chilungamo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova wakwezeka kwambiri pakuti amakhala pamwamba pa zonse adzadzaza Ziyoni ndi chilungamo ndi chipulumutso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova wakwezedwa; pakuti akhala kumwamba; Iye wadzaza Ziyoni ndi ciweruzo ndi cilungamo.