Isaiah 33:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu ao olimba mtima akufuula m'miseu, akazembe odzayesa kudzetsa mtendere akulira kwamphamvu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, olimba mtima ao angofuula kunja, mithenga ya mtendere ilira kowawa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taonani, anthu awo amphamvu akulira mofuwula mʼmisewu; akazembe okhazikitsa mtendere akulira kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, olimba mtima ao angopfuula kunja, mithenga ya mtendere ilira kowawa.