Isaiah 33:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'miseu yaikuluikulu muli zii, palibe odzeramo. Zipangano zaphwanyidwa, mboni zanyozedwa, ndipo palibenso kulemekezana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Njira zamakwalala zikufa, kulibe woyendamo; Asiriya wathyola chipangano, wanyoza midzi, sasamalira anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼmisewu yayikulu mulibe anthu, mʼmisewu mulibe anthu a paulendo. Mdaniyo ndi wosasunga pangano. Iye amanyoza mboni. Palibe kulemekezana.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Njira zamakwalala zikufa, kulibe woyendamo; Asuri watyola cipangano, wanyoza midzi, sasamalira anthu.