Isaiah 34:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mitembo ya anthu ao ophedwa adzangoitaya kunja, nimaola ndi kumanunkha, ndipo mapiri adzafiira ndi magazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ophedwa aonso adzatayidwa kunja, ndipo kununkha kwa mitembo yao kudzamveka, ndipo mapiri adzasungunuka ndi mwazi wao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu awo ophedwa adzatayidwa kunja, mitembo yawo idzawola ndi kununkha; mapiri adzafiira ndi magazi awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ophedwa aonso adzatayidwa kunja, ndipo kununkha kwa mitembo yao kudzamveka, ndipo mapiri adzasungunuka ndi mwazi wao.