Isaiah 36:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mfumuyo ikuti, ‘Musalole kuti Hezekiya akunyengeni, chifukwa sadzatha kukupulumutsani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mfumu itere, Musaleke Hezekiya anyenge inu; pakuti iye sadzathai kukupulumutsani:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zimene mfumu ikunena ndi izi: Musalole kuti Hezekiya akunamizeni. Iye sangakupulumutseni!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mfumu itere, Musaleke Hezekiya anyenge inu; pakuti iye sadzathai kukupulumutsani: