Isaiah 36:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi milungu ya Hamati ndi Aripadi ili kuti tsopano? Nanga milungu ya Sefaravaimu ili kuti? Kodi milunguyo idaupulumutsa mzinda wa Samariya kwa mbuye wanga?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ili kuti milungu ya Hamati, ndi Aripadi? Ili kuti milungu ya Sefaravaimu? Kodi inapulumutsa Samariya m'manja mwanga?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ili kuti milungu ya Hamati ndi Aripadi? Ili kuti milungu ya Sefaravaimu? Kodi inapulumutsa Samariya mʼdzanja langa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iri kuti milungu ya Hamati, ndi Aripadi? iri kuti milungu ya Sefaravaimu? kodi inapulumutsa Samariya m'manja mwanga?