Isaiah 36:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma anthu adangokhala chete osayankhapo kanthu, chifukwa mfumu Hezekiya adaaŵalamula kuti, “Musamuyankhe ai.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iwo anakhala chete, osamuyankha mau, pakuti mfumu inawalamulira kuti, Musamuyankhe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma anthu anakhala chete ndipo sanayankhepo kanthu, chifukwa mfumu inawalamula kuti, “Musayankhe.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iwo anakhala cete, osamuyankha mau, pakuti mfumu inawalamulira kuti, Musamuyankhe.