Isaiah 37:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Chauta, zoonadi mafumu a ku Asiriya adaononga anthu a mitundu ina yonse, nasandutsa maiko ao chipululu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zoonadi, Yehova, mafumu a Asiriya anaononga maiko onse, ndi pokhala pao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Yehova, nʼzoonadi kuti mafumu a Asiriya anawononga mitundu yonse ya anthu ndi mayiko awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zoonadi, Yehova, mafumu a Asuri anaononga maiko onse, ndi pokhala pao.