Isaiah 37:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma Ine ndimadziŵa zonse za iwe pamene ukukhala pansi, pamene ukuyenda kwina ndi kubwerako, ndiponso pamene ukundikwiyira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ndidziwa pokhala pansi pako, ndi kutuluka kwako, ndi kulowa kwako, ndi kundikwiyira kwako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma Ine ndimadziwa zonse za iwe; ndimadziwa pamene ukuyima ndi pamene ukukhala; ndimadziwa pamene ukutuluka ndi pamene ukulowa, ndiponso momwe umandikwiyira Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ndidziwa pokhala pansi pako, ndi kuturuka kwako, ndi kulowa kwako, ndi kundikwiyira kwako.