Isaiah 37:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a m'banja la Yuda amene adzatsalire, adzapezanso bwino, ngati zomera zimene zazimitsa mizu pansi ndi kubala zipatso poyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo otsala amene opulumuka a nyumba ya Yuda adzaphukanso mizu pansi, nadzabala chipatso pamwamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a nyumba ya Yuda amene adzatsalire adzazika mizu yawo pansi ndipo adzabereka zipatso poyera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo otsala amene opulumuka a nyumba ya Yuda adzaphukanso mizu pansi, nadzabala cipatso pamwamba.