Isaiah 38:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndinkaganiza kuti ndizipita ku dziko la akufa, ndidakali mnyamata wabiriŵiri, ndipo kuti ndidzakhala komweko mpakampaka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ine ndinati, Pakati pa masiku anga ndidzalowa m'zipata za kunsi kwa manda; Ndazimidwa zaka zanga zotsala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ine ndinati, Pakati pa masiku anga ndidzalowa m'zipata za kunsi kwa manda; Ndazimidwa zaka zanga zotsala.