Isaiah 38:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndinkaganiza kuti pa dziko lino la anthu amoyo, sindidzaonanso Chauta, anthu okhala pansi pano sindidzaŵapenyanso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinati, Sindidzaona Yehova m'dziko la amoyo; sindidzaonanso munthu pamodzi ndi okhala kunja kuno;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinaganiza kuti, “Sindidzaonanso Yehova, mʼdziko la anthu amoyo, sindidzaonanso mtundu wa anthu kapena kukhala pamodzi ndi amene amakhala pa dziko lapansi lino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinati, Sindidzaona Yehova m'dziko la amoyo; sindidzaonanso munthu pamodzi ndi okhala kunja kuno;