Isaiah 39:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Yesaya adauza Hezekiya kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesaya anati kwa Hezekiya, Imvani mau a Yehova wa makamu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo Yesaya anati kwa Hezekiya, “Imvani mawu a Yehova Wamphamvuzonse:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesaya anati kwa Hezekiya, Imvani mau a Yehova wa makamu.