Isaiah 40:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Atonthozeni mtima, atonthozeni mtima anthu anga,” akutero Mulungu wanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mutonthoze, mutonthoze mtima wa anthu anga, ati Mulungu wanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atonthozeni, atonthozeni anthu anga, akutero Mulungu wanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mutonthoze, mutonthoze mtima wa anthu anga, ati Mulungu wanu.