Isaiah 40:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Woyera Uja akuti, “Kodi mungathe kundiyerekeza ndi yani? Kodi alipo wina wolingana nane?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mudzandifanizira Ine ndi yani tsono, kuti ndilingane naye, ati Woyerayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Woyera uja akuti, “Kodi mudzandiyerekeza Ine ndi yani? Kapena kodi alipo wofanana nane?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mudzandifanizira Ine ndi yani tsono, kuti ndilingane naye, ati Woyerayo.