Isaiah 40:30 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale achinyamata amalefuka ndi kufooka, ngakhale anyamata amaphunthwa ndi kugwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngakhale anyamata adzalefuka ndi kulema ndi amisinkhu adzagwa ndithu:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale achinyamata amalefuka ndi kufowoka, ndipo achinyamata amapunthwa ndi kugwa;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngakhale anyamata adzalefuka ndi kulema ndi amisinkhu adzagwa ndithu: