Isaiah 40:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Udzu umauma, maluŵa amafota, koma mau a Mulungu wathu adzakhalapo mpaka muyaya.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Udzu unyala, duwa lifota, koma mau a Mulungu wathu adzakhala nthawi zachikhalire.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Udzu umanyala ndipo maluwa amafota, koma mawu a Mulungu wathu adzakhalapo mpaka muyaya.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Udzu unyala, duwa lifota, koma mau a Mulungu wathu adzakhala nthawi zacikhalire.