Isaiah 41:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine Chauta ndine amene ndidayambirira kumuuza Ziyoni kuti, ‘Si awo! Akubwera!’ Ndine amene ndidatuma munthu wokanena uthenga wabwinowu ku Yerusalemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Poyamba Ine ndidzati kwa Ziyoni, Taona, taona iwo; ndipo ndidzapereka kwa Yerusalemu wina, amene adza ndi mau abwino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinali woyamba kumuwuza Ziyoni kuti, ‘Taona, si awa akubwera apawa!’ Ndinatumiza mthenga wa nkhani yabwino ku Yerusalemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Poyamba Ine ndidzati kwa Ziyoni, Taona, taona iwo; ndipo ndidzapereka kwa Yerusalemu wina, amene adza ndi mau abwino.