Isaiah 41:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ndikayang'ana, palibe ndi mmodzi yemwe: palibe wotha kulangiza, palibe wotha kuyankha mafunso anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene ndayang'ana, palibe munthu; ngakhale mwa iwo, palibe phungu, amene angathe kuyankha mau, pamene ndiwafunsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ndikayangʼana palibe ndi mmodzi yemwe, palibe ndi mmodzi yemwe pakati pawo wotha kupereka uphungu, palibe woti ayankhe pamene ine ndawafunsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene ndayang'ana, palibe munthu; ngakhale mwa iwo, palibe phungu, amene angathe kuyankha mau, pamene ndiwafunsa.