Isaiah 42:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzaononga mapiri ndi magomo, ndidzaumitsa udzu ndi mitengo yonse kumeneko. Ndidzasandutsa mitsinje kuti ikhale zilumba, ndipo ndidzaumitsa maiŵe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidzapasula mapiri ndi zitunda, ndi kuumitsa zitsamba zao zonse; ndi kusandutsa nyanja zisumbu, ndi kuumitsa matamanda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzawononga mapiri ndi zitunda ndipo ndidzawumitsa zomera zawo zonse; ndidzasandutsa mitsinje kukhala zilumba ndipo ndidzawumitsa maiwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidzapasula mapiri ndi zitunda, ndi kuumitsa zitsamba zao zonse; ndi kusandutsa nyanja zisumbu, ndi kuumitsa matamanda.