Isaiah 42:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Onse amene akhulupirira mafano, amene amatchula mafanowo kuti, ‘Ndinu milungu yathu,’ adzatsitsidwa, ndidzaŵachititsa manyazi kotheratu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwo adzabwezedwa m'mbuyo, adzakhala ndi manyazi ambiri amene akhulupirira mafano osemedwa, nati kwa mafano oyengeka, Inu ndinu milungu yathu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma onse amene amadalira mafano amene amanena kwa mafanowo kuti, ‘ndinu milungu yathu,’ ndidzawachititsa manyazi kotheratu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwo adzabwezedwa m'mbuyo, adzakhala ndi manyazi ambiri amene akhulupirira mafano osemedwa, nati kwa mafano oyengeka, Inu ndinu milungu yathu.