Isaiah 42:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwe waona zambiri, koma zonsezo sudazisamale. Makutu ako ndi otsekuka, koma suumva.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwe waona zinthu zambiri, koma susamalira konse; makutu ako ali otseguka, koma sumva konse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwe waona zinthu zambiri, koma sunazisamale; makutu ako ndi otsekuka koma sumva kanthu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwe waona zinthu zambiri, koma susamalira konse; makutu ako ali otseguka, koma sumva konse.