Isaiah 43:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kale lija Chauta adapanga njira pa nyanja, njira pakati pa madzi amphamvu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atero Yehova, amene akonza njira panyanja, ndi popita m'madzi amphamvu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anapanga njira pa nyanja, anapanga njira pakati pa madzi amphamvu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atero Yehova, amene akonza njira panyanja, ndi popita m'madzi amphamvu;