Isaiah 43:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iyeyo akunena kuti, “Musakumbukire zakale kapena kumaganiziranso zinthu zimene zidachitika kale.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musakumbukire zidapitazo, ngakhale kulingalira zinthu zakale.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Iwalani zinthu zakale; ndipo musaganizirenso zinthu zimene zinachitika kale.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musakumbukire zidapitazo, ngakhale kulingalira zinthu zakale.