Isaiah 43:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amenewo ndi anthu amene ndidadzilengera, ndipo azindiimbira nyimbo zotamanda Ine.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
anthu amene ndinadzilengera ndekha, kuti aonetse matamando anga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu amene ndinadziwumbira ndekha kuti aziyimba nyimbo yotamanda Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
anthu amene ndinadzilengera ndekha, kuti aonetse matamando anga.